1 Corinthians 7:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano ndiyankhe zimene mudandifunsa m'kalata yanu. Nkwabwino kuti munthu asakwatire,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsopano pa zinthu zomwe munandilembera nʼkwabwino kuti munthu asakwatire.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma za izi munalembazi; kuli bwino kwa munthu kusakhudza mkazi.