1 Corinthians 8:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amene amadziyesa wodziŵa kanthu, ndiye kuti sakudziŵabe kwenikweni monga momwe akadayenera kudziŵira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene amaganiza kuti amadziwa kanthu, ndiye kuti sakudziwa monga mmene amayenera kudziwira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati wina ayesa kuti adziwa kanthu sanayambe kudziwa monga ayenera kudziwa.