1 Corinthians 9:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi si koyenerera kwa ife kumalandira chakudya ndi chakumwa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi tilibe ulamuliro wa kudya ndi kumwa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ife tilibe ulamuliro wakudya ndi kumwa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi tiribe ulamuliro wa kudya ndi kumwa?