1 John 1:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tikanena kuti sitidachimwe, tikumuyesa wonama Mulungu, ndipo mau ake sali mwa ife.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tikanena kuti sitidachimwa, timuyesa Iye wonama, ndipo mau ake sakhala mwa ife.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ife tikanena kuti sitinachimwe, tikumutenga Mulungu kukhala wonama, ndipo Mawu ake sali mwa ife.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tikanena kutisitidacimwa, timuyesa iye wonama, ndipo mau ace sakhala mwa ife.