1 John 1:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga, ndipo mwa ife mulibe choona.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tikati kuti tilibe uchimo, tidzinyenga tokha, ndipo mwa ife mulibe choonadi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tikati kuti tiribe ucimo, tidzinyenga tokha, ndipo mwa ife mulibe coonadi.