1 John 4:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye adayamba kutikonda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tikonda ife, chifukwa anayamba Iye kutikonda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye anayamba kutikonda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tikonda ife, cifukwa anayamba iye kutikonda.