1 Kings 1:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Benaya mwana wa Yehoyada adayankha kuti, “Indedi, zichitikedi motero. Chauta, Mulungu wa mbuyanga mfumu, akwaniritse zimenezi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu, nati, Amen, ateronso Yehova Mulungu wa mbuye wanga mfumu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu kuti, “Ameni! Yehova Mulungu wa mbuye wanga mfumu akhazikitse kuti zichitike motero.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu, nati, Amen, ateronso Yehova Mulungu wa mbuye wanga mfumu.