1 Kings 10:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Golide amene ankabwera kwa Solomoni pa chaka chimodzi ankakwanira makilogramu 23,000,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsono kulemera kwake kwa golide anafika kwa Solomoni chaka chimodzi kunali matalente mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi limodzi a golide.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Golide amene Solomoni ankalandira pa chaka ankalemera makilogalamu 23,000,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsono kulemera kwace kwa golidi anafika kwa Solomo caka cimodzi kunali matalenti mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi liimodzi a golidi,