1 Kings 10:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo idauza mfumu Solomoni kuti, “Zimene ndinkamva ndili ku dziko lakwathu, zonena za ntchito zanu ndi nzeru zanu, nzoonadi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati kwa mfumu, Idali yoonadi mbiri ija ndinaimva ine ku dziko langa ya machitidwe anu ndi nzeru zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iyo inati kwa mfumu, “Mbiri imene ndinamva ndili ku dziko kwathu ya zomwe munachita komanso nzeru zanu ndi yoona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa mfumu, idali yoonadi mbiri ija ndinaimva ine ku dziko langa ya macitidwe anu ndi nzeru zanu.