1 Kings 11:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma chifukwa cha Davide bambo wako, sindidzachita zimenezi iwe uli moyo ai. Ndidzaulanda kwa mwana wako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma m'masiku ako sindidzatero chifukwa cha Davide atate wako, koma ndidzaung'ambira m'manja mwa mwana wako;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma chifukwa cha Davide abambo ako, sindidzachita zimenezi iwe uli moyo. Ndidzawugawa mʼdzanja la mwana wako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma m'masiku ako sindidzatero cifukwa ca Davide atate wako, koma ndidzaung'ambira m'manja mwa mwana wako;