1 Kings 15:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo panali nkhondo pakati pa Asa ndi Baasa masiku onse a ufumu wao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali nkhondo pakati pa Asa ndi Baasa mfumu ya Israele masiku ao onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Panali nkhondo pakati pa Asa ndi Baasa mfumu ya Israeli pa nthawi yonse ya ulamuliro wawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali nkhondo pakati pa Asa ndi Basa mfumu ya Israyeli masiku ao onse.