1 Kings 17:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kenaka Eliya adatama Chauta mopemba kuti, “Inu Chauta, Mulungu wanga, kodi mai wamasiyeyu, amene akundisunga, mwamchitiranji choipa chotere, pomuphera mwana wake?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nafuulira kwa Yehova, nati, Yehova Mulungu wanga, kodi mwamgwetsera choipa mkazi wamasiye amene ndikhala naye, kumphera mwanake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka Eliya anafuwula kwa Yehova nati, “Inu Yehova Mulungu wanga, kodi mwabweretsanso choyipa chotere pa mkazi wamasiye amene ine ndikukhala naye, pakuchititsa kuti mwana wake afe?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Napfuulira kwa Yehova, nati, Yehova Mulungu wanga, kodi mwamgwetsera coipa mkazi wamasiye amene ndikhala naye, kumphera mwanace?