1 Kings 17:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adafungatira mwanayo katatu, natamanso Chauta mopemba kuti, “Inu Chauta, Mulungu wanga, mubwezereni moyo wake mwanayu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nafungatira katatu pa mwanayo, nafuulira kwa Yehova, nati, Yehova Mulungu wanga, ndikupemphani, ubwere moyo wake wa mwanayu m'chifuwa mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo Eliya anakumbatira mwanayo katatu ndi kufuwula kwa Yehova kuti, “Inu Yehova Mulungu wanga, mubwezereni mwanayu moyo wake!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nafungatira katatu pa mwanayo, napfuulira kwa Yehova, nati, Yehova Mulungu wanga, ndikupemphanf, ubwere moyo wace wa mwanayu m'cifuwa mwace.