1 Kings 17:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Eliya adatenga mwanayo, natsika naye kuchoka m'chipinda chapamwamba chija, ndipo adampereka kwa mai wake. Tsono adauza maiyo kuti, “Onani, mwana wanu ali moyo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Eliya ananyamula mwanayo, natsika naye ku chipinda chosanja, nalowa naye m'nyumba, nampereka kwa amake; nati, Eliya, Taona, mwana wako ali moyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Eliya ananyamula mwanayo natsika naye kuchoka mʼchipinda chapamwamba chija nalowa naye mʼnyumba. Anamupereka kwa amayi ake ndipo anati, “Taonani, mwana wanu ali ndi moyo!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Eliya ananyamula mwanayo, natsika naye ku cipinda cosanja, nalowa naye m'nyumba, nampereka kwa amace; nati Eliya, Taona, mwana wako ali moyo.