1 Kings 17:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo mai uja adauza Eliya kuti, “Tsopano ndikudziŵa kuti ndinu munthu wa Mulungu, ndipo Chauta walankhula kudzera mwa inu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mkazi anati kwa Eliya, Ndizindikira tsopano kuti ndinu munthu wa Mulungu, ndi kuti mau a Yehova ali m'kamwa mwanuwo ngoona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo mayiyo anati kwa Eliya, “Tsopano ndadziwa kuti ndinu munthu wa Mulungu ndipo mawu a Yehova amene mumayankhula ndi owona.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mkazi anati kwa Eliya, Ndizindikira tsopano kuti ndinu munthu wa Mulungu, ndi kuti mau a Yehova ali m'kamwa mwanuwo ngoona.