1 Kings 17:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Eliyayo adapita nakachita monga momwe Chauta adaanenera. Adapita nakakhala m'mbali mwa mtsinje wa Keriti kuvuma kwa Yordani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Momwemo iye anamuka, nachita monga mwa mau a Yehova, nakakhala kumtsinje Keriti uli ku Yordani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Eliya anachita zomwe Yehova anamuwuza. Anapita ku mtsinje wa Keriti, pafupi ndi Yorodani, nakakhala kumeneko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Momwemo iye anamuka, nacita monga mwa mau a Yehova, nakakhala kumtsinje Keriti uli ku Yordano.