1 Kings 17:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patangopita kanthaŵi, mtsinjewo udaphwa, poti kunalibe mvula m'dzikomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunachitika, atapita masiku ena mtsinje udaphwa, popeza munalibe mvula m'dziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita masiku, mtsinjewo unaphwa chifukwa mvula sinagwe mʼdzikomo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunacitika, atapita masiku ena mtsinje udaphwa, popeza munalibe mvula m'dziko.