1 Kings 18:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patapita nthaŵi yaitali, pa chaka chachitatu cha chilala, Chauta adauza Eliya kuti, “Pita ukadziwonetse kwa Ahabu. Ndidzagwetsa mvula pa dziko lapansi.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo atapita masiku ambiri, mau a Yehova anafika kwa Eliya chaka chachitatu, nati, Kadzionetse kwa Ahabu, ndipo ndidzatumiza mvula padziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita masiku ambiri, mʼchaka chachitatu cha chilala, Yehova anayankhula ndi Eliya kuti, “Pita ukadzionetse kwa Ahabu ndipo ndidzagwetsa mvula pa dziko lapansi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo atapita masiku ambiri, mau a Yehova anafika kwa Eliya caka cacitatu, nati, Kadzionetse kwa Ahabu, ndipo ndidzatumiza mvula padziko.