1 Kings 18:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwina ine ndikangochoka pano, pompo mzimu wa Chauta ukuchotsani kuno kunka nanu komwe ine sindidziŵa. Tsono ndikakamuuza Ahabu, iye osadzakupezani, adzandipha, ngakhale kuti mtumiki wanune ndakhala ndikutumikira Chauta kuyambira ubwana wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzachitika, ine ntakusiyani, mzimu wa Yehova udzakunyamulirani kosakudziwa ine, ndipo ine ntakauza Ahabu, ndipo akalephera kukupezani, adzandipha. Koma ine kapolo wanu ndimaopa Yehova kuyambira ubwana anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine sindikudziwa kumene Mzimu wa Yehova udzakupititsani ine ndikachoka. Ngati ndipita kukamuwuza Ahabu ndipo iye wosadzakupezani, adzandipha. Komatu ine mtumiki wanu ndakhala ndi kupembedza Yehova kuyambira ubwana wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzacitika, ine ntakusiyani, mzimu wa Yehova udzakunyamulirani kosakudziwa ine, ndipo ine ntakauza Ahabu, ndipo akalephera kukupezani, adzandipha. Koma ine kapolo wanu ndimaopa Yehova kuyambira ubwana wanga.