1 Kings 18:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono nthaŵi yamasana ndithu Eliya adayamba kuŵaseka, naŵauza kuti, “Fuulani kwambiri, suja mukuti iyeyo ndi mulungu! Mwina mwaketu watanganidwa, kapena wapita kwina kukadzithandiza, kapena ali pa ulendo, kaya kapena ali m'tulo, ndiye kamdzutsenitu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pausana Eliya anawaseka, nati, Kwezani mau, popeza ndiye mulungu; kapena alikulingirira, kapena wapambuka, kapena ali paulendo, kaya agona, adzagalamuka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi yamasana Eliya anayamba kuwanyogodola ndipo anati, “Fuwulani kwambiri. Ndithudi, iye ndi mulungu! Mwinatu akulingalira kwambiri, kapena watanganidwa, kapena ali paulendo. Mwina wagona ndipo nʼkofunika kuti adzutsidwe.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pausana Eliya anawaseka, nati, Kwezani mau, popeza ndiye mulungu; kapena alikulingirira, kapena wapambuka, kapena ali paulendo, kaya agona, adzagalamuka.