1 Kings 18:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adatenga miyala khumi ndi iŵiri potsata chiŵerengero cha mafuko a ana a Yakobe amene Chauta adaamuuza kuti dzina lake lidzakhala Israele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Eliya anatenga miyala khumi ndi iwiri, monga mwa ziwerengo cha mafuko ana a Yakobo, amene mau a Yehova adamfikira, kuti, Dzina lako ndi Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Eliya anatenga miyala 12, mwala uliwonse kuyimira fuko lililonse la Yakobo, amene Yehova anamuwuza kuti, “Dzina lako lidzakhala Israeli.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Eliya anatenga miyala khumi ndi iwiri, monga mwa ciwerengo ca mafuko a ana a Yakobo, amene mau a Yehova adamfikira, kuti, Dzina lako ndi Israyeli.