1 Kings 18:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndi miyalayo adamangira guwa lotamandirapo Chauta. Tsono adakumba ngalande kuzungulira guwalo. Kukula kwa ngalandeyo kunali ngati moloŵa mitsuko inai ya madzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndi miyalayi anamanga guwa la nsembe m'dzina la Yehova, nazunguniza guwalo ndi mchera, ukulu wake ngati kulandira miyeso iwiri ya mbeu kuzinga guwalo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi miyala imeneyo anamanga guwa mʼdzina la Yehova, ndipo anakumba ngalande yayikulu yolowa malita 15 a madzi kuzungulira guwalo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndi miyalayi anamanga guwa la nsembe m'dzina la Yehova, nazunguniza guwalo ndi mcera, ukulu wace ngati kulandira miyeso iwiri ya mbeu kuzinga guwalo.