1 Kings 18:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mundiyankhe, Inu Chauta, mundiyankhe, kuti anthu aŵa adziŵe kuti Inu Chauta ndinu Mulungu, ndipo kuti atembenuke mtima.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndimvereni Yehova, ndimvereni, kuti anthu awa adziwe kuti Inu Yehova ndinu Mulungu, ndi kuti Inu mwabwezanso mitima yao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndiyankheni, Inu Yehova, ndiyankheni, kuti anthu awa adziwe Inu Yehova, kuti ndinu Mulungu, ndipo kuti mutembenuziranso mitima yawo kwa Inu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndimvereni Yehova, ndimvereni, kuti anthu awa adziwe kuti Inu Yehova ndinu Mulungu, ndi kuti Inu mwabwezanso mitima yao.