1 Kings 18:42 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Ahabu adapita kukachita madyerero. Koma Eliya adakwera pamwamba pa Phiri la Karimele, ndipo adazyolikira pansi naika mutu wake pakati pa maondo ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ahabu anakadya, namwa; koma Eliya anakwera pamwamba pa Karimele, nagwadira pansi, naika nkhope yake pakati pa maondo ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Ahabu anapita kukadya ndi kumwa, koma Eliya anakwera pamwamba pa Phiri la Karimeli, ndipo anawerama mpaka pansi, nayika mutu wake pakati pa mawondo ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ahabu anakadya, namwa; koma Eliya anakwera pamwamba pa Karimeli, nagwadira pansi, naika nkhope yace pakati pa maondo ace.