1 Kings 18:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Ahabu adauza Obadiya kuti, “Tiye tiyendere dziko lonse, tiwone akasupe onse a madzi, ndiponso tipite ku zigwa zonse. Mwina mwake tingapeze udzu womadyetsa akavalo ndi abulu kuti akhale moyo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ahabu anati kwa Obadiya, Kayendere dziko lonse ku zitsime zonse zamadzi, ndi ku mitsinje yonse, kapena tikapeza msipu ndi kusunga moyo wa akavalo ndi nyuru, zingafe nyama zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ahabu anawuza Obadiya kuti, “Pita mʼdziko kulikonse kumene kuli zitsime za madzi ndi ku zigwa zonse. Mwina mwake tingapeze udzu oti nʼkumadyetsa akavalo ndi abulu kuti akhale ndi moyo, kuti tisaphe chiweto chilichonse.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ahabu anati kwa Obadiya, Kayendere dziko lonse ku zitsime zonse zamadzi, ndi ku mitsinje yonse, kapena tikapeza msipu ndi kusunga moyo wa akavalo ndi nyuru, zingafe nyama zonse.