1 Kings 2:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Solomoni adakhala pa mpando waufumu wa Davide atate ake. Ndipo ufumu wake unali wokhazikika kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsono Solomoni anakhala pa mpando wachifumu wa Davide atate wake, ndipo ufumu wake unakhazikika kwakukulu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Solomoni anakhala pa mpando waufumu wa abambo ake Davide, ndipo ufumu wake unakhazikika kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsono Solomo anakhala pa mpando wacifumu wa Davide atate wace, ndipo ufumu wace unakhazikika kwakukuru.