1 Kings 2:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adati, “Koma ndili ndi mau oti ndilankhule nanu.” Bateseba adati, “Lankhula.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anatinso, Ndili nanu mau. Nati iye, Tanena.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo iye anawonjezera kunena kuti, “Ndili ndi mawu oti ndiyankhule nanu.” Batiseba anayankha kuti, “Yankhula.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anatinso, Ndiri nanu mau, Nati iye, Tanena.