1 Kings 21:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
anthuwo adalengeza za kusala zakudya, ndipo adamuika Naboti pa malo aulemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Analalikira kuti asale kudya, naike Naboti pooneka ndi anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo analengeza kuti anthu asale chakudya ndipo anayika Naboti pa malo aulemu pakati pa anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Analalikira kuti asale kudya, naike Naboti pooneka ndi anthu.