1 Kings 21:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yezebele atangomva zakuti Naboti amponya miyala ndipo wafa, adakauza Ahabu kuti, “Dzukani, katengeni munda wamphesa uja umene Naboti Myezireele, ankakukanizani kugula. Nabotiyo sali moyonso ai, wafa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali, atamva Yezebele kuti anamponya Naboti miyala nafa, Yezebele anati kwa Ahabu, Taukani, landirani munda wamphesa wa Naboti Myezireele uja anakana kukugulitsani ndi ndalama, popeza Naboti sali ndi moyo, koma wafa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yezebeli atangomva kuti Naboti amuponya miyala ndipo wafa, iye anakamuwuza Ahabu kuti, “Dzukani, katengeni munda wamphesa wa Naboti wa ku Yezireeli umene anawukaniza kukugulitsani. Naboti sali moyonso, koma wafa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali, atamva Yezebeli kuti anamponya Naboti miyala nafa, Yezebeli anati kwa Ahabu, Taukani, landirani munda wamphesa wa Naboti Myezreeli uja anakana kukugulitsani ndi ndarama, popeza, Naboti sali ndi moyo, koma wafa.