1 Kings 4:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ng'ombe khumi zonenepa zodyetsera m'khola, ng'ombe zakubusa makumi aŵiri, nkhosa 100, osaŵerengera ngondo, nswala, mphoyo ndiponso mbalame zonona zoŵeta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ng'ombe zonenepa khumi, ndi ng'ombe za kubusa makumi awiri, ndi nkhosa zana limodzi, osawerenganso ngondo ndi nswala ndi mphoyo ndi mbalame zoweta.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ngʼombe khumi zonenepa zodyetsera mʼkhola, ngʼombe za ku busa makumi awiri, ndiponso nkhosa ndi mbuzi 100, pamodzinso ndi mbawala, agwape, mphoyo ndi mbalame zoweta zonona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ng'ombe zonenepa khumi, ndi ng'ombe za kubusa makumi awiri, ndi nkhosa zana limodzi, osawerenganso ngondo ndi nswala ndi mphoyo ndi mbalame zoweta.