1 Kings 4:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Solomoni ankalamulira dziko lonse la kuzambwe kwa mtsinje wa Yufurate, kuyambira ku Tifisa mpaka ku Gaza. Mafumu onse akumeneko adamgonjera, choncho Solomoni anali pamtendere ndi maiko ozungulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti analamulira dziko lonse lili tsidya lino la Yufurate, kuyambira ku Tifisa kufikira ku Gaza, inde mafumu onse a ku tsidya lino la Yufurate; nakhala ndi mtendere kozungulira konseko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti ankalamulira dziko lonse la kumadzulo kwa mtsinje wa Yufurate kuyambira ku Tifisa mpaka ku Gaza, mafumu onse a kumadzulo kwa Mtsinje, ndipo anali pa mtendere ndi mayiko onse ozungulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti analamulira dziko lonse liri tsidya lino la Firate, kuyambira ku Tipsa kufikira ku Gaza, inde mafumu onse a ku tsidya tino la Firate; nakhala ndi mtendere kozungulira konseko,