1 Kings 4:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ahisara anali mkulu woyang'anira nyumba ya mfumu. Ndipo Adoniramu, mwana wa Abida, anali mkulu woyang'anira ntchito zathangata.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Ahisara Adoniramu mwana wa Abida anali wamsonkho.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ahisara, anali mkulu woyangʼanira nyumba ya mfumu; Adoniramu mwana wa Abida, anali mkulu woyangʼanira ntchito za thangata.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Ahisara anayang'anira banja la mfumu, ndi Adoniramu mwana wa Abida anali wamsonkho.