1 Kings 5:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Hiramu adapereka kwa Solomoni mitengo yonse ya mkungudza ndi ya paini imene ankakhumbayo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsono Hiramu anapatsa Solomoni mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa monga momwe anafuniramo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero Hiramu anapereka kwa Solomoni mitengo yonse ya mkungudza ndi payini imene ankayifuna,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsono Hiramu anapatsa Solomo mitengo yamkungudza ndi mitengo yamlombwa monga momwe anafuniramo.