1 Kings 5:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Solomoni analinso ndi anthu amtengatenga 70,000, ndi anthu 80,000 osema miyala ku dziko lamapiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Solomoni anawasenzetsa akatundu anthu zikwi makumi asanu ndi awiri, ndi anthu zikwi makumi asanu ndi atatu anatema m'mapiri;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Solomoni anali ndi anthu amtengatenga 70,000, anthu 80,000 osema miyala ku mapiri,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Solomo anawasenzetsa akatundu anthu zikwi makumi asanu ndi awiri, ndi anthu zikwi makumi asanu ndi atatu anatema m'mapiri;