1 Kings 5:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake tsono, mulamule anthu anu kuti andidulire mikungudza ya ku Lebanoni. Tsono anthu anga adzagwira ntchito pamodzi ndi anthu anuwo, ndipo ine ndidzakulipirani chifukwa cha anthu anu malipiro amene mungatchule. Inu mukudziŵa kuti pakati pathupa, palibe munthu wodziŵa kudula mitengo ngati Asidoni.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsono, lamulirani kuti anditemere mitengo yamkungudza ku Lebanoni, ndipo akapolo anga adzakhala ndi akapolo anu, ndipo ndidzakupatsani mphotho ya akapolo anu monga mudzanena; popeza mudziwa kuti pakati pa ife palibe mmisiri wakudziwa kutema mitengo ngati anthu a ku Sidoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Choncho lamulani kuti andidulire mikungudza ya ku Lebanoni. Anthu anga adzagwira ntchito imeneyo pamodzi ndi anthu anuwo, ndipo ine ndidzalipira anthu anuwo malipiro amene inu mungakhazikitse. Inu mukudziwa kuti ife tilibe anthu aluso locheka matabwa monga Asidoni.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsono, lamulirani kuti anditemere mitengo yamkungudza ku Lebano, ndipo akapolo anga adzakhala ndi akapolo anu, ndipo ndidzakupatsani mphotho ya akapolo anu monga mudzanena; popeza mudziwa kuti pakati pa ife palibe mmisiri wakudziwa kutema mitengo ngati anthu a ku Sidoni.