1 Kings 6:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adatsirizanso zipinda zosanjikana kuzungulira Nyumbayo. Chipinda chilichonse msinkhu wake unali ngati mamita aŵiri, ndipo adazilumikiza ku Nyumbayo ndi mitanda yamkungudza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamanga zipindazo zogundana ndi nyumba yonseyo, chipinda chilichonse msinkhu wake mikono isanu; ndipo anazilumikizitsa kunyumba ndi mitengo yamkungudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Msinkhu wa chipinda chilichonse unali mamita awiri, ndipo anazilumukiza ku Nyumbayo ndi mitanda yamkungudza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamanga zipindazo zogundana ndi nyumba yonseyo, cipinda ciri conse msinkhu wace mikono isanu; ndipo anazilumikizitsa kunyumba ndi mitengo yamkungudza.