1 Kings 6:36 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adamanganso bwalo lam'kati. Makoma ake adapanga ndi miyala yosema mizere itatu, mosinthanitsana ndi mzere umodzi wa matabwa amkungudza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo bwalo la m'kati analimanga mizere itatu ya miyala yosemasema, ndi mzere umodzi wa mitanda yamkungudza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo anamanga bwalo la mʼkati lokhala ndi khoma lokhala ndi mizere itatu ya miyala yosema ndiponso mzere umodzi wa matabwa osemedwa a mkungudza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo bwalo la m'kati analimanga mizere itatu ya miyala yosemasema, ndi mzere umodzi wa mitanda yamkungudza.