1 Kings 8:60 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho anthu a mitundu yonse ya pa dziko lapansi adziŵe kuti Chauta ndiye Mulungu, palibenso wina.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti anthu onse a pa dziko lapansi akadziwe kuti Yehova ndiye Mulungu, palibe wina.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kotero kuti anthu a mitundu yonse pa dziko lapansi adziwe kuti Yehova ndi Mulungu ndipo kuti palibenso wina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti anthu onse a pa dziko lapansi akadziwe kuti Yehova ndiye Mulungu, palibe wina.