1 Peter 1:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzikhala ngati ana omvera, osatsatanso zimene munkalakalaka pamene munali osadziŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
monga ana omvera osadzifanizitsanso ndi zilakolako zakale, pokhala osadziwa inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga ana omvera, musatsatenso zilakolako zoyipa zomwe munali nazo pamene munali osadziwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
monga ana omvera osadzifanizitsanso ndi zilakolako zakale, pokhala osadziwa inu;