1 Peter 1:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja mau a Mulungu akuti, “Muzikhala oyera mtima popeza kuti Ineyo ndine woyera mtima.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
popeza kwalembedwa, Muzikhala oyera mtima, pakuti Ine ndine woyera mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti, kwalembedwa kuti, “Khalani oyera mtima, chifukwa Ine ndine Woyera.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
popeza kwalembedwa, Muzikhala oyera mtima, pakuti Ine ndine woyera mtima.