1 Peter 2:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
popeza kuti mwachilaŵadi chifundo cha Ambuye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ngati mwalawa kuti Ambuye ali wokoma mtima;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pakuti tsopano mwalawadi kuti Ambuye ndi wabwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ngati mwalawa kuti Ambuye ali wokoma mtima;