1 Peter 3:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
popeza kuti adzadziwonera okha makhalidwe anu aulemu ndi angwiro.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuona mayendedwe anu oyera ndi kuopa kwanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pamene aona moyo wanu wachiyero ndi moyo woopa Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuona mayendedwe anu oyera ndi kuopa kwanu.