1 Peter 4:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chimalizo cha zonse chayandikira. Nchifukwa chake khalani ochenjera ndi odziletsa, kuti muthe kupemphera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma chitsiriziro cha zinthu zonse chili pafupi; chifukwa chake khalani anzeru, ndipo dikirani m'mapemphero;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chimaliziro cha zinthu zonse chili pafupi. Choncho khalani maso ndi odziletsa kuti muthe kupemphera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma citsiriziro ca zinthu zonse ciri pafupi; cifukwa cace khalani anzeru, ndipo dikirani m'mapemphero;