1 Samuel 1:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Hanayo ankavutika kwambiri mumtima mwake, ndipo adapemphera kwa Chauta, akulira ndi mtima woŵaŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mkaziyo anali ndi mtima wowawa, napemphera kwa Yehova, naliratu misozi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Hana anavutika mʼmoyo mwake, ndipo anapemphera kwa Yehova akulira kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mkaziyo anali ndi mtima wowawa, napemphera kwa Yehova, naliratu misozi;