1 Samuel 1:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adamufunsa kuti, “Mai, kodi mukhala chiledzerere mpaka liti? Pitani, akayambe watha vinyo mwamwayu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Eli anati kwa iye, Udzaleka liti kuledzera? Chotsa vinyo wako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo anamufunsa Hana kuti, “Kodi mukhala chiledzerere mpaka liti? Pitani, ayambe wakuchokani vinyo mwamwayo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Eli anati kwa iye, Udzaleka liti kuledzera? cotsa vinyo wako.