1 Samuel 13:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Afilisti adatuma kagulu kankhondo kukalonda mpata wa Mikimasi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono gulu lina lankhondo la Chifilisti linapita kukalonda mpata wa Mikimasi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anaturuka kunka ku mpata wa ku Mikimasi.