1 Samuel 15:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndikumva chisoni kuti ndidampatsa ufumu Saulo. Wabwerera m'mbuyo, waleka kunditsata, ndipo sadamvere malamulo anga.” Pamenepo Samuele adapsa mtima, ndipo adadandaula kwa Chauta usiku wonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kundichititsa chisoni kuti ndinaika Saulo akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanachite malamulo anga. Ndipo Samuele anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndikumva chisoni chifukwa ndinayika Sauli kukhala mfumu. Wabwerera mʼmbuyo, waleka kunditsata ndipo sanamvere malangizo anga.” Samueli anapsa mtima, ndipo analira kwa Yehova usiku wonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kundicititsa cisoni kuti ndinaika Sauli akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanacita malamulo anga, Ndipo Samueli anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.