1 Samuel 17:49 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adapisa dzanja m'thumba natulutsamo mwala, ndipo adauponya namlasa pa mphumi Mfilistiyo. Mwalawo udamuloŵa m'mutu, ndipo Mfilistiyo adagwa pansi chafufumimba.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Davide anapisa dzanja lake m'thumba mwake, natulutsamo mwala, nauponya, nalasa Mfilistiyo pamphumi; ndi mwalawo unalowa m'mphumi, ndipo iye anagwa pansi chafufumimba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Davideyo anapisa dzanja lake mʼthumba lake natengamo mwala ndipo anawuponya, nalasa pa mphumi pa Mfilisitiyo. Mwalawo unalowa pa chipumi chake, ndipo anagwa chafufumimba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Davide anapisa dzanja lace m'thumba mwace, naturutsamo mwala, nauponya, nalasa Mfilistiyo pamphumi; ndi mwalawo unalowa m'mphumi, ndipo iye anagwa pansi cafufumimba.