1 Samuel 22:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono aliyense amene anali pa mavuto, kapena anali ndi ngongole, kapena anali wosakondwa, onsewo adasonkhana kwa Davide. Iyeyo ankaŵatsogolera. Onse anali ngati anthu 400 pamodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo yense wosautsidwa, ndi yense wa ngongole, ndi yense wowawidwa mtima, anaunjikana kwa iye; iye nakhala mtsogoleri wao; ndipo anali nao anthu ngati mazana anai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo aliyense amene anali pa mavuto, kapena ndi ngongole kapenanso amene anali wosakondwa anasonkhana kwa iye, ndipo iye anakhala mtsogoleri wawo. Onse pamodzi analipo amuna 400.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo yense wosautsidwa, ndi yense wa ngongole, ndi yense wowawidwa mtima, anaunjikana kwa iye; iye nakhala mtsogoleri wao; ndipo anali nao anthu ngati mazana anai.