1 Samuel 27:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Davide adakhala ku dziko la Afilisti chaka chimodzi ndi miyezi inai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kuwerenga kwake kwa masiku Davide anakhala ku dziko la Afilisti ndiko chaka chimodzi ndi miyezi inai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Davide anakhala mʼdziko la Afilisti kwa chaka chimodzi ndi miyezi inayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kuwerenga kwace kwa masiku Davide anakhala ku dziko la Afilisti ndiko caka cimodzi ndi miyezi inai.